Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 16:26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pamwamba pa izi, pakati pa ife ndi inu pakhazikika phompho lalikuru, kotero kuti iwo akufuna kuoloka kucokera kuno kunka kwa inu sangathe, kapena kucokera kwanuko kuyambuka kudza kwa ife, sangathenso.

Werengani mutu wathunthu Luka 16

Onani Luka 16:26 nkhani