Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 16:15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anati kwa iwo, Inu ndinu odziyesera nokha olungama pamaso pa anthu; koma Mulungu azindikira mitima yanu; cifukwa ici cimene cikuzika mwa anthu ciri conyansa pamaso pa Mulungu.

Werengani mutu wathunthu Luka 16

Onani Luka 16:15 nkhani