Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 15:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pakufika kunyumba kwace amema abwenzi ace ndi anansi ace, nanena nao, Kondwerani ndi ine, cifukwa ndinapeza nkhosa yanga yotayikayo.

Werengani mutu wathunthu Luka 15

Onani Luka 15:6 nkhani