Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 12:37 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Odala akapolowo amene mbuye wao, pakudza iye, adzawapeza odikira; indetu ndinena ndinu, kuti iye adzadzimangira m'cuuno, nadzawakhalitsa pansi kudya, nadzafika, nadzawatumikira.

Werengani mutu wathunthu Luka 12

Onani Luka 12:37 nkhani