Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 11:52-54 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

52. 3 Tsoka inu, acilamulo! cifukwa munacotsa cifungulo ca nzeru; inu simunalowamo nokha, ndipo munawaletsa iwo analinkulowa.

53. Ndipo pamene iye anaturuka m'menemo, alembi ndi Afarisi anayamba kumuumiriza iye kolimba, ndi kumtompha iye ndi zinthu zambiri;

54. 4 namlindira akakole kanthu koturuka m'kamwa mwace.

Werengani mutu wathunthu Luka 11