Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 11:29 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo pakusonkhana pamodzi makamu a anthu, anayamba kunena, Mbadwo uno ndi mbadwo woipa; ufuna cizindikilo, ndipo cizindikilo sicidzapatsidwa kwa uwu koma cizindikilo ca Yona.

Werengani mutu wathunthu Luka 11

Onani Luka 11:29 nkhani