Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 10:6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo mukakhala mwana wa mtendere m'menemo, mtendere wanu udzapumula pa iye; koma ngati mulibe, udzabwerera kwa inu.

Werengani mutu wathunthu Luka 10

Onani Luka 10:6 nkhani