Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 10:21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Nthawi yomweyo iye anakondwera ndi Mzimu Wovera, nati, Ndikubvomerezani Inu, Atate, Ambuye wa kumwamba ndi wa dziko, kuti izi munazibisira anzeru ndi ozindikira, ndipo munaziululira ana amakanda; indedi, Atate, pakuti kotero kudakondweretsa pamaso panu.

Werengani mutu wathunthu Luka 10

Onani Luka 10:21 nkhani