Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 1:74-77 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

74. Kutipatsa ife kuti titalanditsidwa ku dzanja la adani athu,17 Tidzamtumikira iye, opanda mantha,

75. 18 M'ciyero ndi cilungamo pamaso pace, masiku athu onse.

76. 19 Eya, ndipo iwetu kamwanawe, udzanenedwa mneneri wa Wamkulukulu:20 Pakuti udzatsogolera Ambuye, kukonza njira zace;

77. Kuwapatsa anthu ace adziwitse cipulumutso,21 Ndi makhululukidwe a macimoao,

Werengani mutu wathunthu Luka 1