Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 1:70-76 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

70. 15 (Monga iye analankhula ndi m'kamwa mwa aneneri ace oyera mtima, a kale lomwe),

71. Cipulumutso ca adani athu, ndi pa dzanja la anthu onse amene atida ife;

72. 16 Kucitira atate athu cifundo, Ndi kukumbukila pangano lace lopatulika;

73. Cilumbiro cimene iye anacilumbira kwa Abrahamu atate wathu,

74. Kutipatsa ife kuti titalanditsidwa ku dzanja la adani athu,17 Tidzamtumikira iye, opanda mantha,

75. 18 M'ciyero ndi cilungamo pamaso pace, masiku athu onse.

76. 19 Eya, ndipo iwetu kamwanawe, udzanenedwa mneneri wa Wamkulukulu:20 Pakuti udzatsogolera Ambuye, kukonza njira zace;

Werengani mutu wathunthu Luka 1