Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 1:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo adzamtsogolera iye, ndi mzimu ndi mphamvu ya Eliya, kutembenuzira mitima ya atate kwa ana ao, ndi osamvera kuti atsate nzeru ya olungama mtima; kukonzeratu Ambuye anthu okonzeka.

Werengani mutu wathunthu Luka 1

Onani Luka 1:17 nkhani