Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Luka 1:13 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma mngelo anati kwa iye, Usaope Zakariya, cifukwa kuti lamveka pemphero lako, ndipo mkazi wako adzakubalira mwana wamwamuna, ndipo udzamucha dzina lace Yohane.

Werengani mutu wathunthu Luka 1

Onani Luka 1:13 nkhani