20. Inde, mbale, ndikondwere nawe mwa Ambuye: utsitsimutse mtima wanga mwa Kristu.
21. Pokhulupirira kumvera kwako ndikulembera iwe, podziwa kuti udzacicanso koposa cimene ndinena.
22. Koma undikonzerenso pogona; pakuti ndiyembekeza kuti mwa mapemphero anu ndidzapatsidwa kwa inu.
23. Epafra wandende mnzanga mwa Kristu Yesu akulankhula iwe;
24. ateronso, Marko, Aristarko, Dema, Luka, anchito anzanga.