Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Filemoni 1:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. PAULO, wandende wa Kristu Yesu, ndi Timoteo mbaleyo, kwa Filemoni wokondedwayo ndi wanchito mnzathu,

2. ndi kwa Apiya mlongoyo, ndi Arkipo msilikari mnzathu, ndi kwa Mpingo uli m'nyumba yako;

3. Cisomo kwa inu ndi mtendere za kwa Mulungu Atate wathu ndi Ambuye Yesu Kristu.

4. Ndiyamika Mulungu wanga nthawi zonse, ndi kukumbukila iwe m'mapemphero anga,

Werengani mutu wathunthu Filemoni 1