Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 6:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo anapatsa yense wa iwo mwinjiro woyera; nanena kwa iwo, kuti apumulebe kanthawi, kufikira atakwaniranso akapolo anzao, ndi abale ao amene adzaphedwa monganso iwo eni.

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 6

Onani Cibvumbulutso 6:11 nkhani