Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 21:11 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

ndipo unakhala nao ulemerero wa Mulungu; kuunika kwace kunafanana ndi mwala wa mtengo wace woposa, Dgati mwala wayaspi, wonyezimira, ngati krustalo;

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 21

Onani Cibvumbulutso 21:11 nkhani