Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 21:1-2 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Ndipo ndinaona m'mwamba mwatsopano ndi dziko latsopano; pakuti m'mwamba moyamba ndi dziko loyamba zidaeoka, ndipo kulibenso nyanja.

2. Ndipo ndinaona mzinda woyerawo, Yerusalemu watsopano, ulikutsika Kumwamba kwa Mulungu, wokonzeka ngati mkwatibwi wokometsedwera mwamuna wace.

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 21