Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 2:17 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Iye wakukhala nalo khutu amve cimene Mzimu anena kwa Mipingo. Kwa iye wolakika, ndidzampatsa mana obisika, ndipo ndidzampatsa mwala woyera, ndi pa mwalawo dzina latsopano lolembedwapo, wosalidziwa munthu ali yense koma iye wakuulandira.

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 2

Onani Cibvumbulutso 2:17 nkhani