Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 17:10-12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

10. ndipo ali mafumu asanu ndi awiri asanu adagwa, imodzi iriko, yinayo siinadze; ndipo pamene ifika iyenera iyo kukhala kanthawi.

11. Ndipo cirombo cinalico, ndi kulibe, ico comwe nelieo cacisanu ndi citatu, ndipo ciri mwa zisanu ndi ziwirizo, nicimuka kucitayiko.

12. Ndipo nyanga khumi udaziona ndiwo mafumu khumi, amene sanalandire ufumu; koma alandira ulamuliro ngati mafumu, ora limodzi, pamodzi ndi cirombo.

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 17