Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Cibvumbulutso 10:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo ndinamuka kwa mngelo, ndi kunena naye, Ndipatse kabukuko. Ndipo ananena ndi ine, Dzatenge, nudye; ndipo kadzawawitsa m'mimbamwako, komatu m'kamwa mwako kadzazuna ngati uci.

Werengani mutu wathunthu Cibvumbulutso 10

Onani Cibvumbulutso 10:9 nkhani