Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Aroma 9:14-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

14. Ndipo tsono tidzatani? Kodi ciripo cosalungama ndi Mulungu? Msatero ai.

15. Pakuti anati ndi Mose, Ndidzacitira cifundo amene ndimcitira cifundo, ndipo ndidzakhala ndi cisoni kwa iye amene ndikhala naye cisoni.

16. Cotero sicifuma kwa munthu amene afuna, kapena kwa iye amene athamanga, koma kwa Mulungu amene acitira cifundo.

Werengani mutu wathunthu Aroma 9