Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Aroma 8:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma inu simuli m'thupi ai, koma mumzimu, ngatitu Mzimu wa Mulungu akhalabe mwa inu. Koma ngati munthu alibe Mzimu wa Kristu, siali wace wa Kristu.

Werengani mutu wathunthu Aroma 8

Onani Aroma 8:9 nkhani