Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Aroma 8:37-39 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

37. Koma 13 m'zonsezi, ife tilakatu, mwa iye amene anatikonda.

38. Pakuti ndakopeka mtima kuti ngakhale imfa, ngakhale moyo, ngakhale angelo, ngakhale maufumu, ngakhale zinthu ziripo, ngakhale zinthu zirinkudza, ngakhale zimphamvu,

39. ngakhale utali, ngakhale kuya, ngakhale colengedwa cina ciri conse, sicingadzakhoze kutisiyanitsa ife ndi cikondi ca Mulungu, cimene ciri mwa Kristu Yesu Ambuye wathu.

Werengani mutu wathunthu Aroma 8