1. Ndipo potero Myuda aposa Dinji? Kapena mdulidwe upindulanji?
2. Zambiri monse monse: coyamba, kuti mau a Mulungu anaperekedwa kwa iwo.
3. Nanga bwanji ngati ena sanakhulupira? Kodi kusakhulupira kwao kuyesa cabe cikhulupiriko ca Mulungu?
4. Msatero ai. Koma Mulungu akhale woona, ndimo anthu onse akhale onama; monga kwalembedwa,Kuti Inu mukayesedwe wolungama m'maneno anu,Ndi kuti mukalakike m'mene muweruzidwa.