Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Aroma 16:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo kwa iye amene ali wamphamvu yakukhazikitsa inu monga mwa uthenga wanga wabwino, ndi kulalildra kwa Yesu Kristu, monga mwa bvumbulutso la cinsinsi cimene cinabisika mwa nthawi zonse zosayamba,

Werengani mutu wathunthu Aroma 16

Onani Aroma 16:25 nkhani