Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Aroma 16:13-16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

13. Mulankhule Rufo, wosankhidwayo mwa Ambuye, ndi amai wace ndi wanga.

14. Mulankhule Asunkrito, Felego, Herme, Patroba, Henna ndi abale amene ali nao.

15. Mulankhule Filologo ndi Yuliya, Nerea ndi mlongo wace, ndi Olumpa, ndi oyeramtima onse ali pamodzi nao.

16. Mulankhulane wina ndi mnzace ndi kupsompsona kopatulika. Mipingo yonse ya Kristu ikulankhulani inu.

Werengani mutu wathunthu Aroma 16