Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Aroma 15:2-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

2. Yense wa ife akondweretse mnzace, kumcitira zabwino, zakumlimbikitsa.

3. Pakuti Kristunso sanadzikondweretsa yekha; koma monga kwalembedwa, Minyozo ya iwo amene anakuoyoza iwe Inagwa pa Ine,

4. Pakuti zonse zinalembedwa kale zinalembedwa kutilangiza, kuti mwa cipiriro ndi citonthozo ca malembo, tikhale ndi ciyembekezo.

5. Ndipo Mulungu wa cipiriro ndi wa citonthozo apatse inu kuti mukhale ndi mtima umodzi wina ndi mnzace, monga mwa Kristu Yesu;

Werengani mutu wathunthu Aroma 15