Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Aroma 12:18-21 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

18. Ngati nkutheka, monga momwe mukhoza, khalani ndi mtendere ndi anthu onse.

19. Musabwezere coipa, okondedwa, koma patukani pamkwiyo; pakuti kwalembedwa, Kubwezera kuli kwanga, Ine ndidzabwezera, ati Ambuye.

20. Koma ngati mdani wako akumva njala, umdyetse, ngati akumva ludzu, ummwetse; pakuti pakutero udzaunjika makala a mota pamutu pace.

21. Musagonje kwa coipa, koma ndi cabwino genietsani coipa.

Werengani mutu wathunthu Aroma 12