Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Aroma 11:2-5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

2. Mulungu sanataya anthu ace amene iye anawadziwiratu, Kapena simudziwa kodi cimene lembo linena za Eliya? kuti anaumirira Mulungu poneneza Israyeli, kuti,

3. Ambuye, anawapha aneneri anu, nagwetsa maguwa anu a nsembe; ndipo ine ndatsala ndekha, ndipo alikufuna moyo wanga.

4. Koma kuyankha kwa Mulungu kudatani kwa iye? Ndinadzisiyira ndekha anthu amunazikwi zisanu ndi ziwiri, amene sanagwadira Baala.

5. Coteronso nthawi yatsopano ciripo cotsalira monga mwa kusankha kwa cisomo.

Werengani mutu wathunthu Aroma 11