Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Akolose 4:15-18 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

15. Lankhulani abalewo a m'Laodikaya, ndi Numfa, ndi Mpingowo wa m'nyumba yao.

16. Ndipo pamene mudamwerenga kalata uyu, amwerengenso mu Mpingo wa ku Laodikaya, ndi inunso muwerenge wa ku Laodikaya,

17. Ndipo nenani kwa Arkipo, Samaliratu utumiki umene udaulandira mwa Ambuye, kuti uukwanitse.

18. Kulankhula ndi dzanja langa, kwa ine Paulo. Kumbukilani zoo mangira zanga, Cisomo cikhale nanu.

Werengani mutu wathunthu Akolose 4