Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Akolose 3:1-4 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

1. Cifukwa cace ngati munaukitsidwa pamodzi ndi Kristu, funani zakumwamba, kumene kuli Kristu wokhala pa dzanja lamanja la Mulungu.

2. Lingalirani zakumwamba osati za padziko ai.

3. Pakuti munafa, ndipo moyo wanu wabisika pamodzi ndi Kristu mwa Mulungu,

4. Pamene Kristu adzaoneka, ndiye moyo wathu, pamenepo inunso mudzaonekera pamodzi ndi iye m'ulemerero.

Werengani mutu wathunthu Akolose 3