Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ahebri 8:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

amene atumikira cifaniziro ndi mthunzi wa zakumwambazo monga Mose acenjezedwa m'mene anafuna kupanga cihema: pakuti, Cenjera, ati, ucite zonse monga mwa citsanzoco caonetsedwa kwa iwe m'phiri.

Werengani mutu wathunthu Ahebri 8

Onani Ahebri 8:5 nkhani