Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ahebri 7:23-26 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

23. Ndipo iwo ndiwo ambiri anakhala ansembe, popeza imfa idawaletsa asakhalebe;

24. koma iye cifukwa kuti akhala iye nthawi yosatha ali nao unsembe wosasinthika,

25. kucokera komwekoakhoza kupulumutsa konse konse iwo akuyandikira kwa Mulungu mwa iye, popeza ali nao moyo wace cikhalire wa kuwapembedzera iwo.

26. Pakuti mkulu wa ansembe wotere anatiyenera ife, woyera mtima, wopanda coipa, wosadetsedwa, wosiyana ndi ocimwa, wakukhala wopitirira miyamba;

Werengani mutu wathunthu Ahebri 7