Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ahebri 6:10 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

pakuti Mulungu sali wosalungama kuti adzaiwala nchito yanu, ndi cikondico mudacionetsera ku dzina lace, umo mudatumikira oyera mtima ndi kuwatumikirabe.

Werengani mutu wathunthu Ahebri 6

Onani Ahebri 6:10 nkhani