Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ahebri 4:5-8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

5. Ndipo m'menemonso,Ngati adzalowa mpumulo wanga.

6. Popeza tsono patsala kuti ena akalowa momwemo, ndi iwo amene Uthenga Wabwino unalalikidwa kwa iwo kale sanalowamo cifukwa ca kusamvera,

7. alangizanso tsiku lina, ndi kunena m'Davide, itapita nthawi yaikuru yakuti, Lero, monga kwanenedwakale,Lero ngati mudzamva mau ace,Musaumitse mitima yanu.

8. Pakuti ngati Yoswa akadawapumitsa iwo, sakadalankhuia m'tsogolomo za tsiku lina.

Werengani mutu wathunthu Ahebri 4