Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ahebri 12:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Penyani musakane wolankhulayo. Pakuti ngati iwowa sanapulumuka, pomkana iye amene anawacenjeza padziko, koposatu sitidzapulumuka ife, odzipatulira kwa iye wa Kumwamba;

Werengani mutu wathunthu Ahebri 12

Onani Ahebri 12:25 nkhani