Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ahebri 10:35-39 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

35. Potero musataye kulimbika kwanu, kumene kuli naco cobwezera mphotho cacikuru.

36. Pakuti cikusowani cipiriro, kuti 8 pamene mwacita cifuniro ca Mulungu, mukalandire lonjezano.

37. 9 Pakuti katsala kanthawi kakang'onong'ono,Ndipowakudzayoadzafika, wesacedwa.

38. 10 Koma wolungama wangayo adzakhala ndi moyo wocokera m'cikhulupiriro:Ndipo ngati abwerera, moyo wanga ulibe kukondwera mwaiye.

39. Koma ife si ndife 11 a iwo akubwerera kulowa citayiko; koma 12 a iwo a cikhulupiriro ca ku cipulumutso ca moyo.

Werengani mutu wathunthu Ahebri 10