Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Ahebri 1:5 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti kwa mngelo uti anati nthawi iri yonse,Iwe ndiwe Mwana wanga,Lero ine ndakubala Iwe?ndiponso,Ine ndidzakhala kwa iye Atate,Ndipo iye adzakhala kwa ine Mwana?

Werengani mutu wathunthu Ahebri 1

Onani Ahebri 1:5 nkhani