Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Agalatiya 6:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Pakuti wakufesera kwa thupi la iye yekha, cocokera m'thupi adzatuta cibvundi; koma wakufesera kwa Mzimu, cocokera mu Mzimu adzatuta moyo wosatha.

Werengani mutu wathunthu Agalatiya 6

Onani Agalatiya 6:8 nkhani