Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Agalatiya 6:14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma kudzitamandira ine konse konse, iai, koma mu mtanda wa Ambuye wathu Yesu Kristu, amene mwa iye dziko lapansi lapacikidwira ine, ndi ine ndapacikidwira dziko lapansi.

Werengani mutu wathunthu Agalatiya 6

Onani Agalatiya 6:14 nkhani