Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Agalatiya 5:12-15 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

12. Mwenzi atadzidula, iwo akugwedezetsani inu.

13. Pakuti adakuitanani inu, abale, mukhale mfulu; cokhaco musacite nao ufulu wanu cothandizira thupi, komatu mwa cikondi citiranani ukapolo.

14. Pakuti mau amodzi akwaniritsa cilamulo conse ndiwo; Uzikonda mnzako monga udzikonda iwe mwini.

15. Koma ngati mulumana ndi kudyana, cenjerani mungaonongane.

Werengani mutu wathunthu Agalatiya 5