Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Agalatiya 3:2-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

2. ici cokha ndifuna kuphunzira kwa inu, Kodi munalandira Mzimuyo ndi nchito za lamulo, kapena ndi kumva kwa cikhulupiriro?

3. Kodi muli opusa otere? Popeza mudayamba ndi Mzimu, kodi tsopano mutsiriza ndi thupi?

4. Kodi mudamva zowawa zambiri zotere kwacabe? ngatitu kwacabe.

5. Ndipo iye amene akuonjezerani inu Mzimuyo, nacita zimphamvu mwa inu, atero kodi ndi nchito za lamulo, kapena ndi kumva kwa cikhulupiriro?

6. Monga Abrahamu anakhulupirira Mulungu, ndipo kunawerengedwa kwa iye cilungamo,

Werengani mutu wathunthu Agalatiya 3