Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Afilipi 2:25 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Koma ndinayesa nkufunika kutuma kwa inu Epafrodito mbaleyo, ndiye wanchito mnzanga ndi msilikari mnzanga, ndiye mtumwi wanu, ndi wonditumikira pa cosowa canga;

Werengani mutu wathunthu Afilipi 2

Onani Afilipi 2:25 nkhani