Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Aefeso 4:2-6 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

2. ndi kuonetsera kudzicepetsa konse, ndi cifatso, ndi kuonetsera cipiriro, ndi kulolerana wina ndi mnzace, mwa cikondi;

3. ndi kusamalitsa kusunga umodzi wa Mzimu mwa cimangiriro ca mtendere.

4. Thupi limodzi ndi Mzimu mmodzi, monganso anakuitanani m'ciyembekezo cimodzi ca maitanidwe anu;

5. Ambuye mmodzi, cikhulupiriro cimodzi, ubatizo umodzi,

6. Mulungu mmodzi ndi Atate wa onse amene ali pamwamba pa onse, ndi mwa onse, ndi m'kati mwa zonse.

Werengani mutu wathunthu Aefeso 4