Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

Aefeso 4:16 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

kucokera mwa Iye thupi lonse, lokowanidwa ndi lolumikizidwa pamodzi, pothandizanapo mfundo yonse, monga mwa kucititsa kwa ciwalo conse pa muyeso wace, licita makulidwe a thupi, kufikira cimango cace mwa cikondi.

Werengani mutu wathunthu Aefeso 4

Onani Aefeso 4:16 nkhani