Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Timoteo 4:11-14 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

11. Luka yekha ali pamodzi ndi ine. Umtenge Marko, adze pamodzi ndi iwe; pakuti ayenera kunditumikira.

12. Koma Tukiko ndamtuma ku Efeso.

13. Copfunda cija ndinacisiya ku Trowa kwa Karpo, udze naco pakudza iwe, ndi mabuku, makamaka zikopa zija zolembedwa.

14. Alesandro wosula mkuwa anandicitira zoipa zambiri: adzambwezera iye Ambuye monga mwa nchito zace;

Werengani mutu wathunthu 2 Timoteo 4