Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Timoteo 3:8 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Ndipo monga momwe Yane ndi Yambre anatsutsana naye Mose, kotero iwonso atsutsana naco coonadi; ndiwo anthu obvunditsitsa mtima, osatsimikizidwa pacikhulupiriro.

Werengani mutu wathunthu 2 Timoteo 3

Onani 2 Timoteo 3:8 nkhani