Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

2 Akorinto 13:10-12 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

10. Cifukwa ca ici ndilembera izi pokhala palibe ine, kuti pokhala ndiri pomwepo ndingacite mowawitsa, monga mwa ulamuliro umene Ambuye anandipatsa ine wakumangirira, ndipo si wakugwetsa.

11. Cotsalira, abale, kondwerani, Mucitidwe angwiro; mutorithozedwe; khalani a mtima umodzi, khalani mumtendere; ndipo Mulungu wa cikondi ndi mtendere akhale pamodzi ndi inu.

12. Lankhulanani ndi cipsompsono copatulika.

Werengani mutu wathunthu 2 Akorinto 13