Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Yohane 4:9 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Umo cidaoneka cikondi ca Mulungu mwa ife, kuti Mulungu anamtuma Mwana wace wobadwa yekha alowe m'dziko lapansi, kuti tikhale ndi moyo mwa iye.

Werengani mutu wathunthu 1 Yohane 4

Onani 1 Yohane 4:9 nkhani