Chipangano Chakale

Chipangano Chatsopano

1 Yohane 4:1 Buku Lopatulika 1992 (BL92)

Okondedwa, musamakhulupirira mzimu uli wonse, koma yesani mizimu ngati icokera mwa Mulungu: popeza aneneri onyenga ambiri anaturuka kulowa m'dziko lapansi.

Werengani mutu wathunthu 1 Yohane 4

Onani 1 Yohane 4:1 nkhani